Levitiko 18:12 - Buku Lopatulika12 Usamavula mlongo wa atate wako; ndiye wa chibale cha atate wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Usamavula mlongo wa atate wako; ndiye wa chibale cha atate wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Usagone ndi mlongo wa bambo wako, poti ameneyo ndi thupi limodzi ndi bambo wako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “ ‘Usagonane ndi mlongo wa abambo ako; popeza ameneyo ndi thupi limodzi ndi abambo ako. Onani mutuwo |