Levitiko 18:11 - Buku Lopatulika11 Usamavula mwana wamkazi wa mkazi wa atate wako, amene anambala atate wako, ndiye mlongo wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Usamavula mwana wamkazi wa mkazi wa atate wako, amene anambala atate wako, ndiye mlongo wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Usagone ndi mwana wamkazi wa mkazi wa bambo wako amene bambo wakoyo adabala, poti ameneyo ndi mlongo wako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “ ‘Usagonane ndi mwana wamkazi wa mkazi wa abambo ako, amene abambo akowo anabereka; popeza ameneyo ndi mlongo wako. Onani mutuwo |