Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 18:10 - Buku Lopatulika

10 Usamavula mwana wamkazi wa mwana wamwamuna wako, kapena mwana wamkazi wa mwana wamkazi wako; pakuti thupi lao ndi lako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Usamavula mwana wamkazi wa mwana wamwamuna wako, kapena mwana wamkazi wa mwana wamkazi wako; pakuti thupi lao ndi lako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Usagone ndi mdzukulu wako, mwana wa mwana wako wamwamuna, kapena mdzukulu wako, mwana wa mwana wako wamkazi, chifukwa kuteroko nkudzivula.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 “ ‘Usagonane ndi mdzukulu wako: mwana wa mwana wako wamwamuna kapena mwana wa mwana wako wamkazi. Kutero nʼkudzichotsa ulemu.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 18:10
2 Mawu Ofanana  

Usamavula mwana wamkazi wa mkazi wa atate wako, amene anambala atate wako, ndiye mlongo wako.


Usamavula mlongo wako, mwana wamkazi wa atate wako, kapena mwana wamkazi wa mai wako, wobadwa kwanu, kapena wobadwa kwina.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa