Levitiko 17:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo wansembeyo awaze mwaziwo paguwa la nsembe la Yehova, pa khomo la chihema chokomanako, natenthe mafuta akhale fungo lokoma lokwera kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo wansembeyo awaze mwaziwo pa guwa la nsembe la Yehova, pa khomo la chihema chokomanako, natenthe mafuta akhale fungo lokoma lokwera kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo wansembe awaze magazi ake pa guwa la Chauta, pakhomo pa chihema chamsonkhano. Atatero atenthe mafuta ake, kuti atulutse fungo lokomera Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Wansembe awaze magazi ake pa guwa la Yehova limene lili pa khomo la tenti ya msonkhano ndipo atenthe mafuta ake kuti atulutse fungo lokomera Yehova. Onani mutuwo |