Levitiko 17:16 - Buku Lopatulika16 Koma akapanda kuzitsuka, kapena kusamba thupi lake, adzasenza mphulupulu yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma akapanda kuzitsuka, kapena kusamba thupi lake, adzasenza mphulupulu yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma akapanda kuchapa zovalazo, kapena akapanda kusamba thupi lonse, adzasenza machimo ake.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Koma ngati sachapa zovala zake ndi kusamba, adzasenzabe machimo ake.’ ” Onani mutuwo |