Levitiko 16:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Aroni abwere nayo mbuzi imene adaigwera maere a Yehova, naiyese nsembe yauchimo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Aroni abwere nayo mbuzi imene adaigwera maere a Yehova, naiyese nsembe yauchimo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Aroniyo abwere ndi mbuzi imene maere aonetsa kuti ndi ya Chauta, ndipo aipereke kuti ikhale nsembe yopepesera machimo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Aaroni abwere ndi mbuzi imene maere aonetsa kuti ndi ya Yehova, ndipo apereke kuti ikhale nsembe yopereka chifukwa cha tchimo. Onani mutuwo |