Levitiko 16:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo ku khamu la ana a Israele atenge atonde awiri akhale a nsembe yauchimo, ndi nkhosa yamphongo imodzi ikhale ya nsembe yopsereza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo ku khamu la ana a Israele atenge atonde awiri akhale a nsembe yauchimo, ndi nkhosa yamphongo imodzi ikhale ya nsembe yopsereza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Aroniyo atenge atonde aŵiri ochokera ku mpingo wa Aisraele, kuti akhale nsembe yopepesera machimo, ndi nkhosa imodzi yamphongo kuti ikhale nsembe yopsereza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kuchokera pa gulu la Aisraeli, Aaroni azitenga mbuzi zazimuna ziwiri kuti zikhale nsembe yopepesera machimo ndi nkhosa yayimuna kuti ikhale nsembe yopsereza. Onani mutuwo |