Levitiko 15:28 - Buku Lopatulika28 Koma akayeretsedwa kukha kwake, adziwerengere masiku asanu ndi awiri, ndipo atatero adzakhala woyeretsedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Koma akayeretsedwa kukha kwake, adziwerengere masiku asanu ndi awiri, ndipo atatero adzakhala woyeretsedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Atatha matenda a kusamba kwakeko, mkazi aŵerenge masiku asanu ndi aŵiri, ndipo pambuyo pake akhala woyeretsedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 “ ‘Nthawi yosamba ikatha, mkaziyo awerenge masiku asanu ndi awiri, ndipo masikuwo akatha adzakhala woyeretsedwa. Onani mutuwo |