Levitiko 15:18 - Buku Lopatulika18 Mkazi yemwe, mwamuna atagona naye, onse awiri asambe ndi madzi, nadzakhala odetsedwa kufikira madzulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Mkazi yemwe, mwamuna atagona naye, onse awiri asambe ndi madzi, nadzakhala odetsedwa kufikira madzulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Mwamuna akataya mbeu yake pogona ndi mkazi, onse aŵiriwo asambe, koma akhalabe oipitsidwa mpaka madzulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mwamuna akagona ndi mkazi wake nataya mbewu yake yaumuna, onse awiriwo asambe. Komabe adzakhala odetsedwa mpaka madzulo. Onani mutuwo |