Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 15:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo zotengera zadothi wazikhudza wakukhayo, aziphwanye; ndi zamtengo, azitsuke ndi madzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo zotengera zadothi wazikhudza wakukhayo, aziphwanye; ndi zamtengo, azitsuke ndi madzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Chiŵiya chadothi chimene munthu wotulutsa mafinyayo akhudze, achiphwanye, ndipo chiŵiya chilichonse chamtengo achitsuke m'madzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 “ ‘Mʼphika wadothi umene munthu wotulutsa mafinyayo wakhudza awuphwanye, ndipo chiwiya chilichonse chamtengo achitsuke ndi madzi.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 15:12
10 Mawu Ofanana  

Udzawathyola ndi ndodo yachitsulo; udzawaphwanya monga mbiya ya woumba.


iitana posonkhana anthu polowera pachipata; m'mzinda inena mau ake,


Tembenukani pamene ndikudzudzulani; taonani, nditsanulira pa inu mzimu wanga, ndikudziwitsani mau anga.


Mwananga, zisachokere kumaso ako; sunga nzeru yeniyeni ndi kulingalira;


Ndipo munthu aliyense wakukhayo akamkhudza, osasambatu m'manja m'madzi, atsuke zovala zake, nasambe m'madzi, nadzakhala wodetsedwa kufikira madzulo.


Chikonzeke pachiwaya ndi mafuta; udze nacho chokazinga; chopereka chaufa chazidutsu ubwere nacho, chikhale fungo lokoma la kwa Yehova.


Ndipo mphika wadothi umene anaphikamo nyamayi auswe, koma ngati anaiphika mu mphika wamkuwa, atsuke uwu, nautsukuluze ndi madzi.


Pakuti tidziwa kuti ngati nyumba ya pansi pano ya msasa wathu ipasuka, tili nacho chimango cha kwa Mulungu, ndiyo nyumba yosamangidwa ndi manja, yosatha, mu Mwamba.


amene adzasanduliza thupi lathu lopepulidwa, lifanane nalo thupi lake la ulemerero, monga mwa machitidwe amene akhoza kudzigonjetsera nao zinthu zonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa