Levitiko 15:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo munthu aliyense wakukhayo akamkhudza, osasambatu m'manja m'madzi, atsuke zovala zake, nasambe m'madzi, nadzakhala wodetsedwa kufikira madzulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo munthu aliyense wakukhayo akamkhudza, osasambatu m'manja m'madzi, atsuke zovala zake, nasambe m'madzi, nadzakhala wodetsedwa kufikira madzulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Aliyense amene munthu wotulutsa mafinyayo amkhudze asanasambe m'manja, achape zovala zake, ndipo asambe thupi lonse, koma akhalabe woipitsidwa mpaka madzulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “ ‘Munthu wotulutsa mafinyayo akakhudza munthu aliyense asanasambe mʼmanja, wokhudzidwayo achape zovala zake ndi kusamba. Komabe adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Onani mutuwo |