Levitiko 14:7 - Buku Lopatulika7 nawaze kasanu ndi kawiri iye amene akuti amyeretse khate lake, namutche woyera, nataye mbalame yamoyo padambo poyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 nawaze kasanu ndi kawiri iye amene akuti amyeretse khate lake, namutche woyera, nataye mbalame yamoyo padambo poyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono wansembe awaze magazi kasanu ndi kaŵiri pa munthu amene akuti amuyeretse khateyo. Pamenepo wodwalayo amutche kuti ndi woyeretsedwa, ndipo aiwulutsire ku thengo mbalame yamoyoyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Wansembe awaze magazi kasanu ndi kawiri pa munthu woti amuyeretse khateyo ndipo alengeze kuti munthuyo ndi woyeretsedwa. Kenaka wansembe awulutsire ku thengo mbalame yamoyoyo. Onani mutuwo |