Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 14:57 - Buku Lopatulika

57 kulangiza tsiku loti chikhala chodetsa, ndi tsiku loti chikhala choyera; ichi ndi chilamulo cha khate.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

57 kulangiza tsiku loti chikhala chodetsa, ndi tsiku loti chikhala choyera; ichi ndi chilamulo cha khate.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

57 Malamulo ameneŵa ngonena za chinthu choipitsidwa ndi chosaipitsidwa. Atsatidwe pa nthenda zonse za khate.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

57 kuti mudziwe ngati chinthucho ndi choyeretsedwa kapena chodetsedwa. Amenewa ndiwo malamulo a nthenda zonse za khate.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 14:57
7 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake atero Yehova, Ukabwerera pamenepo ndidzakubwezanso, kuti uime pamaso panga; ndipo ukasiyanitsa cha mtengo wake ndi chonyansa, udzakhala ngati m'kamwa mwanga; ndipo adzabwerera kwa iwe, koma sudzabwerera kwa iwo.


Ndipo aziphunzitsa anthu anga asiyanitse pakati pa zopatulika ndi zinthu wamba, ndi kuwazindikiritsa pakati pa zodetsa ndi zoyera.


ndi kuti musiyanitse pakati pa zopatulika ndi zinthu wamba, ndi pakati pa zodetsedwa ndi zoyera;


Ichi ndi chilamulo cha nthenda yakhate ili pa chovala chaubweya kapena chathonje, ngakhale pamuyaro, kapena pamtsendero, kapena pa chinthu chilichonse chopangika ndi chikopa; kuchitcha choyera kapena kuchitcha chodetsa.


ndi yachotupa, ndi yankhanambo, ndi yachikanga;


Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,


Chenjerani nayo nthenda yakhate, kusamaliratu, ndi kuchita monga mwa zonse akuphunzitsani ansembe Alevi; monga ndinalamulira iwo, momwemo muzisamalira kuchita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa