Levitiko 14:57 - Buku Lopatulika57 kulangiza tsiku loti chikhala chodetsa, ndi tsiku loti chikhala choyera; ichi ndi chilamulo cha khate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201457 kulangiza tsiku loti chikhala chodetsa, ndi tsiku loti chikhala choyera; ichi ndi chilamulo cha khate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa57 Malamulo ameneŵa ngonena za chinthu choipitsidwa ndi chosaipitsidwa. Atsatidwe pa nthenda zonse za khate. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero57 kuti mudziwe ngati chinthucho ndi choyeretsedwa kapena chodetsedwa. Amenewa ndiwo malamulo a nthenda zonse za khate. Onani mutuwo |