Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 14:54 - Buku Lopatulika

54 Ichi ndi chilamulo cha nthenda iliyonse yakhate, ndi yamfundu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 Ichi ndi chilamulo cha nthenda iliyonse yakhate, ndi yamfundu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 Izi ndizo zimene muyenera kuchita ngati muona kuti

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 Amenewa ndiwo malamulo a nthenda ya khate, bala lonyerenyetsa,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 14:54
16 Mawu Ofanana  

Ichi ndi chilamulo cha nyama, ndi cha mbalame, ndi cha zamoyo zonse zakuyenda m'madzi, ndi cha zamoyo zonse zakukwawa pansi;


ndipo wansembe aione nthenda pa khungu la thupi; ndipo ngati tsitsi la panthenda lasanduka la mbuu, ndi nthenda ikaoneka yapitirira khungu la thupi lake, ndiyo nthenda yakhate; ndipo wansembe amuone, namutche wodetsedwa.


Chilamulo cha wakhate tsiku la kumyeretsa kwake ndi ichi: azidza naye kwa wansembe;


Ichi ndi chilamulo cha iye ali ndi nthenda yakhate, wosakhoza kufikana nazo zofunika pomyeretsa pake.


Koma ataye mbalame yamoyo kunja kwa mzinda kuthengo koyera; motero aichitire choitetezera nyumbayo; ndipo idzakhala yoyera.


Ichi ndi chilamulo cha wakukha, ndi cha iye wakugona uipa, kuti kumkhalitse wodetsedwa;


Ndipo chilamulo cha chopereka chaufa ndicho: ana a Aroni azibwera nacho pamaso pa Yehova ku guwa la nsembe.


Lankhula ndi Aroni ndi ana ake, ndi kuti, Chilamulo cha nsembe yauchimo ndi ichi: Pamalo pophera nsembe yopsereza ndipo pophera nsembe yauchimo pamaso pa Yehova; ndiyo yopatulika kwambiri.


Uza Aroni ndi ana ake, ndi kuti, Chilamulo cha nsembe yopsereza ndi ichi: nsembe yopsereza izikhala pa nkhuni za paguwa la nsembe usiku wonse kufikira m'mawa; ndipo moto wa paguwa la nsembe uziyakabe pamenepo.


Ndipo chilamulo cha nsembe yopalamula ndi ichi: ndiyo yopatulika kwambiri.


Icho ndi chilamulo cha nsembe yopsereza, cha nsembe yaufa, cha nsembe yauchimo, ndi cha nsembe yopalamula, ndi cha kudzaza dzanja, ndi cha nsembe zoyamika;


Chilamulo ndi ichi: Munthu akafa m'hema, yense wakulowa m'hemamo, ndi yense wakukhala m'hemamo, adzakhala wodetsedwa masiku asanu ndi awiri.


Ichi ndi chilamulo cha nsanje, pamene mkazi, pokhala naye mwamuna wake, ampatukira nadetsedwa;


Ndipo chilamulo cha Mnaziri, atatha masiku a kusala kwake ndi ichi: azidza naye ku khomo la chihema chokomanako;


Chenjerani nayo nthenda yakhate, kusamaliratu, ndi kuchita monga mwa zonse akuphunzitsani ansembe Alevi; monga ndinalamulira iwo, momwemo muzisamalira kuchita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa