Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 14:5 - Buku Lopatulika

5 ndipo wansembe auze kuti aphe mbalame imodzi m'mbale yadothi pamwamba pamadzi oyenda;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 ndipo wansembe auze kuti aphe mbalame imodzi m'mbale yadothi pamwamba pa madzi oyenda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Wansembeyo alamule anthuwo kuti mbalame imodzi aiphere m'mbale yadothi pamwamba pa madzi atsopano.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Wansembe alamule anthuwo kuti mbalame imodzi ayiphere mu mʼphika wa dothi pamwamba pa madzi abwino.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 14:5
8 Mawu Ofanana  

pamenepo wansembe auze kuti amtengere iye wakuti akonzedwe, mbalame ziwiri zoyera zamoyo, ndi mtengo wamkungudza, ndi ubweya wofiira, ndi hisope;


naphe mbalame imodzi m'mbale yadothi, pamwamba pamadzi oyenda;


natenge mbalame yamoyo, ndi mtengo wamkungudza, ndi ubweya wofiira, ndi hisope, naziviike pamodzi ndi mbalame yamoyo m'mwazi wa mbalame adaipha pamwamba pamadzi oyenda;


natenge madzi opatulika m'mbale yadothi wansembeyo, natengeko fumbi lili pansi mu chihema, wansembeyo nalithire m'madzimo.


pakuti anapachikidwa mu ufooko, koma ali ndi moyo mu mphamvu ya Mulungu. Pakuti ifenso tili ofooka mwa Iye, koma tidzakhala ndi moyo pamodzi ndi Iye, mu mphamvu ya Mulungu, ya kwa inu.


Koma tili nacho chuma ichi m'zotengera zadothi, kuti ukulu woposa wamphamvu ukhale wa Mulungu, wosachokera kwa ife;


Pakuti tidziwa kuti ngati nyumba ya pansi pano ya msasa wathu ipasuka, tili nacho chimango cha kwa Mulungu, ndiyo nyumba yosamangidwa ndi manja, yosatha, mu Mwamba.


Popeza tsono ana ndiwo a mwazi ndi nyama, Iyenso momwemo adalawa nao makhalidwe omwewo kuti mwa imfa akamuononge iye amene anali nayo mphamvu ya imfa, ndiye mdierekezi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa