Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 14:44 - Buku Lopatulika

44 pamenepo wansembe alowe naonemo, ndipo taonani, ngati nthenda yakula m'nyumba, ndiyo khate lonyeka m'nyumba; ndiyo yodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 pamenepo wansembe alowe naonemo, ndipo taonani, ngati nthenda yakula m'nyumba, ndiyo khate lonyeka m'nyumba; ndiyo yodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 wansembe apite kukayang'ana. Zikakhala kuti zafalikiranso m'nyumbamo, ndiye kuti ndere zomwe zidafalikira m'nyumbamo ndi zoopsa. Nyumbayo njoipitsidwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 wansembe apite kukayionetsetsenso ndipo ngati nderezo zafalikira mʼnyumbamo, ndiye kuti ndere zimenezo ndi zoopsa. Nyumba imeneyo ndi yodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 14:44
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ikabweranso nthenda, nibukanso m'nyumba atagumula miyala, ndipo atapala m'nyumba namatanso;


Ndidzalitulutsa ili, ati Yehova wa makamu, ndipo lidzalowa m'nyumba ya wakuba, ndi m'nyumba ya iye wolumbira monama pa dzina langa; ndipo lidzakhala pakati pa nyumba yake, ndi kuitha pamodzi ndi mitengo yake ndi miyala yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa