Levitiko 14:41 - Buku Lopatulika41 napalitse nyumba m'kati monsemo, natayire ku malo akuda kunja kwa mzinda dothi adapalako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 napalitse nyumba m'kati monsemo, natayire ku malo akuda kunja kwa mudzi dothi adapalako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Pambuyo pake wansembe auze anthu kuti apale makoma onse m'kati mwa nyumbayo, ndipo dothi akupalalo akalitaye ku dzala kunja kwa mzinda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Wansembe awuze anthu kuti apale makoma onse a mʼkati mwa nyumbayo, ndipo zopalidwazo akazitaye ku malo odetsedwa a kunja kwa mudzi. Onani mutuwo |