Levitiko 14:40 - Buku Lopatulika40 pamenepo wansembe auze kuti agumule miyalayi pali nthenda, naitayire ku malo akuda kunja kwa mzinda; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 pamenepo wansembe auze kuti agumule miyalayi pali nthenda, naitayire ku malo akuda kunja kwa mudzi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 wansembeyo alamule kuti anthu agamule miyala m'mene muli nderezo, ndipo akaitaye ku dzala kunja kwa mzinda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 wansembe alamule kuti anthu agumule miyala imene muli nderezo ndipo akayitaye kudzala la kunja kwa mzinda. Onani mutuwo |