Levitiko 14:32 - Buku Lopatulika32 Ichi ndi chilamulo cha iye ali ndi nthenda yakhate, wosakhoza kufikana nazo zofunika pomyeretsa pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ichi ndi chilamulo cha iye ali ndi nthenda yakhate, wosakhoza kufikana nazo zofunika pomyeretsa pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Limeneli ndilo lamulo la munthu wakhate amene alibe zinthu zoperekera kuyeretsedwa kwake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 “Amenewa ndi malamulo a munthu wakhate amene alibe zinthu zoti apereke pamene akuyeretsedwa. Onani mutuwo |