Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 14:26 - Buku Lopatulika

26 ndipo wansembe athireko mafuta aja m'chikhato chake chamanzere cha iye mwini;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 ndipo wansembe athireko mafuta aja m'chikhato chake chamanzere cha iye mwini;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Kenaka wansembe athireko mafuta m'dzanja lake lamanzere,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Kenaka wansembe athire mafuta mʼdzanja lake lamanzere,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 14:26
2 Mawu Ofanana  

naphe mwanawankhosa wa nsembe yopalamula, ndipo wansembe atengeko mwazi wa nsembe yopalamula, naupake pa ndewerere ya khutu la ku dzanja lamanja la iye akuti ayeretsedwe, ndi pa chala chachikulu cha dzanja lake lamanja, ndi pa chala chachikulu cha phazi lake la ku dzanja lamanja;


ndipo wansembe awazeko mafuta aja ali m'dzanja lake lamanzere ndi chala chake cha dzanja lamanja, kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa