Levitiko 14:2 - Buku Lopatulika2 Chilamulo cha wakhate tsiku la kumyeretsa kwake ndi ichi: azidza naye kwa wansembe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Chilamulo cha wakhate tsiku la kumyeretsa kwake ndi ichi: azidza naye kwa wansembe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Lamulo la munthu wakhate pa tsiku la kuyeretsedwa kwake nali: Abwere naye kwa wansembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Malamulo a munthu wakhate pa tsiku la kuyeretsedwa kwake ndi awa: Abwere naye kwa wansembe. Onani mutuwo |