Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:54 - Buku Lopatulika

54 pamenepo wansembe aziuza kuti atsuke chija pali khate, nachibindikiritse masiku asanu ndi awiri ena;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 pamenepo wansembe aziuza kuti atsuke chija pali khate, nachibindikiritse masiku asanu ndi awiri ena;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 wansembeyo alamule kuti achape chovalacho, ndipo achiike padera masiku asanu ndi aŵiri ena.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 iye alamulire kuti chinthu choyipitsidwacho achichape. Akatero achiyike padera kwa masiku enanso asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:54
2 Mawu Ofanana  

Ndipo wansembe akaona, ndipo taonani, nthenda njosakula pachovala, kapena pamuyaro, kapena pamtsendero, kapena pa chinthu chilichonse chopangika ndi chikopa;


ndipo wansembe aone nthenda ataitsuka, ndipo taonani, ngati nthendayi siinasandulike maonekedwe ake, yosakulanso nthenda, ndicho chodetsedwa; uchitenthe ndi moto; ndilo funka, kungakhale kuyera kwake kuli patsogolo kapena kumbuyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa