Levitiko 13:48 - Buku Lopatulika48 ngakhale ili pamuyaro, kapena pamtsendero, chathonje, kapena chaubweya, ngakhale ili pa chikopa, kapena pa chinthu chilichonse chopanga ndi chikopa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 ngakhale ili pamuyaro, kapena pamtsendero, chathonje, kapena chaubweya, ngakhale ili pa chikopa, kapena pa chinthu chilichonse chopanga ndi chikopa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 kapena nsalu yathonje kapena yaubweya, kapenanso chikopa kapena chinthu chilichonse chopangidwa ndi chikopa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 kaya ndi chovala chopangidwa ndi nsalu yathonje kapena yaubweya, yoluka ndi thonje kapena ubweya, yachikopa kapena yopangidwa ndi chikopa, Onani mutuwo |