Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:47 - Buku Lopatulika

47 Ndiponso ngati nthenda yakhate ili pa chovala chaubweya, kapena chathonje;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Ndiponso ngati nthenda yakhate ili pa chovala chaubweya, kapena chathonje;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 “Chovala chaubweya kapena chathonje chikakhala ndi nguwi

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 “Nsalu iliyonse ikakhala ndi nguwi,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:47
13 Mawu Ofanana  

Maukonde ao sadzakhala zovala, sadzafunda ntchito zao; ntchito zao zili ntchito zoipa, ndi chiwawa chili m'manja mwao.


Pakuti ife tonse takhala ngati wina amene ali wosakonzeka; ndi zolungama zathu zonse zili ngati chovala chodetsedwa; ndipo ife tonse tifota monga tsamba, ndi zoipa zathu zitiuluza monga mphepo.


Ndipo unatengako zovala zako, ndi kudzimangira misanje ya mawangamawanga, ndi kuchitapo chigololo; zotere sizinayenere kufika kapena kuchitika.


Masiku onse nthenda ikali pa iye azikhala wodetsedwa; ali wodetsedwa, agone pa yekha pokhala pake pakhale kunja kwa chigono.


ngakhale ili pamuyaro, kapena pamtsendero, chathonje, kapena chaubweya, ngakhale ili pa chikopa, kapena pa chinthu chilichonse chopanga ndi chikopa;


Ndipo atenthe chovalacho ngakhale muyaro wake, ngakhale mtsendero wake, chaubweya kapena chathonje, kapena chilichonse chachikopa chili ndi khate, ndilo khate lofetsa; achitenthe ndi moto.


Ichi ndi chilamulo cha nthenda yakhate ili pa chovala chaubweya kapena chathonje, ngakhale pamuyaro, kapena pamtsendero, kapena pa chinthu chilichonse chopangika ndi chikopa; kuchitcha choyera kapena kuchitcha chodetsa.


ndi ya khate la chovala, ndi la nyumba;


Usiku wapita, ndi mbandakucha wayandikira; chifukwa chake tivule ntchito za mdima, ndipo tivale zida za kuunika.


kuti muvule, kunena za makhalidwe anu oyamba, munthu wakale, wovunda potsata zilakolako za chinyengo;


Pakuti munafa, ndipo moyo wanu wabisika pamodzi ndi Khristu mwa Mulungu.


koma ena muwapulumutse ndi kuwakwatula kumoto; koma ena muwachitire chifundo ndi mantha, nimudane naonso malaya ochitidwa mawanga ndi thupi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa