Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:44 - Buku Lopatulika

44 ndiye wakhate, ndiye wodetsedwa; wansembe amutchetu wodetsedwa; nthenda yake ili pamutu pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 ndiye wakhate, ndiye wodetsedwa; wansembe amutchetu wodetsedwa; nthenda yake ili pamutu pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 ndiye kuti munthuyo ndi woipitsidwa ndithu. Wansembe ayenera kumtchula kuti ndi woipitsidwa, ali ndi khate lakumutu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 ndiye kuti munthuyo ali ndi khate, motero ndi wodetsedwa. Wansembe alengeze kuti munthuyo ndi wodetsedwa chifukwa cha chithupsa cha pamutu pakepo.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:44
7 Mawu Ofanana  

Iwowa akufa akali biriwiri, ndi moyo wao utayika ngati odetsedwa.


Nanga bwanji mukali chimenyedwere kuti inu mulikupandukirabe? Mutu wonse ulikudwala, ndi mtima wonse walefuka.


Pamenepo wansembe azimuona, ndipo taonani, ngati chotupa chake cha nthenda chili chotuuluka pa dazi la pamutu wake, kapena la pamphumi pake, monga maonekedwe a khate pa khungu la thupi;


Ndipo azing'amba zovala zake za wakhate ali ndi nthendayo, ndi tsitsi la pamutu pake lizikhala lomasuka, naphimbe iye mlomo wake wa m'mwamba, nafuule, Wodetsedwa, wodetsedwa!


Koma ngati diso lako lili loipa, thupi lako lonse lidzakhala lodetsedwa. Chifukwa chake ngati kuwala kumene kuli mwa inu kuli mdima, mdimawo ndi waukulu ndithu!


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa