Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:42 - Buku Lopatulika

42 Koma ngati pali nthenda yotuuluka pakati pa dazi lake la pamutu, kapena la pamphumi, ndipo khate lilikubuka pakati pa dazi lake la pamutu, kapena la pamphumi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 Koma ngati pali nthenda yotuuluka pakati pa dazi lake la pamutu, kapena la pamphumi, ndipo khate lilikubuka pakati pa dazi lake la pamutu, kapena la pamphumi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Koma pa dazi lapankhongo kapena lapamphumi pakakhala banga la nthenda loyera mofiirira, limenelo ndi khate limene likutuluka pa nkhongo kapena pa mphumi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Koma ngati pa dazi la pamutu kapena la pa chipumi pakhala chithupsa choyera mofiirira, ndiye kuti ndi khate limenelo lochokera mu dazi la pamutu lija kapena pa chipumi lija.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:42
5 Mawu Ofanana  

ndipo padali chilonda pali chotupa choyera, kapena chikanga chotuuluka, pamenepo achionetse kwa wansembe; ndipo wansembe aone,


Ngati munthu ali nacho chotupa, kapena nkhanambo, kapena chikanga pa khungu la thupi lake, ndipo isandulika nthenda yakhate pa khungu la thupi lake, azifika kwa Aroni wansembe, kapena kwa mmodzi wa ana ake ansembe;


Ndipo ngati tsitsi lathothoka pamphumi pake ndiye wa masweswe, koma woyera.


Pamenepo wansembe azimuona, ndipo taonani, ngati chotupa chake cha nthenda chili chotuuluka pa dazi la pamutu wake, kapena la pamphumi pake, monga maonekedwe a khate pa khungu la thupi;


naone nthendayo, ndipo taonani, nthenda ikakhala yosumbudzuka m'makoma a nyumba yobiriwira kapena yofiira, ndipo maonekedwe ake yakumba kubzola khoma;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa