Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:41 - Buku Lopatulika

41 Ndipo ngati tsitsi lathothoka pamphumi pake ndiye wa masweswe, koma woyera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 Ndipo ngati tsitsi lathothoka pamphumi pake ndiye wa masweswe, koma woyera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Munthu akakhala wopanda tsitsi pa mphumi ndiponso m'litsipa, ndiye kuti ali ndi dazi lapamphumi, koma ndi wosaipitsidwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Ngati tsitsi lake layoyoka chapamphumi ndiye kuti ndi dazi la pa chipumi limenelo koma munthuyo ndi woyera.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:41
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati tsitsi la munthu lathothoka, ndiye wadazi; koma woyera.


Koma ngati pali nthenda yotuuluka pakati pa dazi lake la pamutu, kapena la pamphumi, ndipo khate lilikubuka pakati pa dazi lake la pamutu, kapena la pamphumi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa