Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:30 - Buku Lopatulika

30 wansembe aziona nthenda; ndipo taonani, ngati ioneka yokumba kubzola khungu, ndipo pali tsitsi loyezuka lotetemera; pamenepo wansembe amutche wodetsedwa; ndiyo mfundu, ndilo khate la mutu kapena ndevu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 wansembe aziona nthenda; ndipo taonani, ngati ioneka yokumba kubzola khungu, ndipo pali tsitsi loyezuka lotetemera; pamenepo wansembe amutche wodetsedwa; ndiyo mfundu, ndilo khate la mutu kapena ndevu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 wansembe aiwonetsetse nthendayo. Ikaoneka kuti ikuzama, ndipo ubweya ukakhala wachikasu ndi wotetemera, wansembeyo amutchule wodwalayo kuti ndi woipitsidwa. Imeneyo ndi mfundu yonyerenyesa, khate lakumutu kapenanso lakundevu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 wansembe aonetsetse balalo ndipo likaoneka kuti lazama, ndipo ubweya wa pamalopo wasanduka wachikasu ndi wonyololoka, wansembe alengeze kuti munthuyo ndi wodetsedwa. Zimenezo ndi mfundu zonyerenyetsa, khate lakumutu kapena ku chibwano.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:30
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati mwamuna kapena mkazi ali ndi nthenda pamutu kapena pandevu,


Ndipo wansembe akaona nthenda yamfundu, ndipo taonani, ioneka yosakumba kubzola khungu, ndipo palibe tsitsi lakuda pamenepo, wansembe ambindikiritse iye ali ndi mfundu masiku asanu ndi awiri;


ndipo tsiku lachisanu ndi chiwiri wansembe aone nthendayi; ndipo taonani, ngati mfundu njosakula, ndipo mulibe tsitsi loyezuka, ndipo mfundu ikaoneka yosakumba kubzola khungu,


Ichi ndi chilamulo cha nthenda iliyonse yakhate, ndi yamfundu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa