Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:24 - Buku Lopatulika

24 Kapena pamene thupi lidapsa ndi moto pakhungu pake, ndipo mnofu wofiira wakupsawo usanduka chikanga chotuuluka, kapena chotuwa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Kapena pamene thupi lidapsa ndi moto pakhungu pake, ndipo mnofu wofiira wakupsawo usanduka chikanga chotuuluka, kapena chotuwa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 “Munthu akakhala ndi bala lamoto, ndipo chilonda cha balalo chikasanduka banga loyera mofiirira kapena loyera kumene,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 “Munthu akakhala ndi bala lamoto pa khungu lake, ndipo chilonda cha balalo chikasanduka banga loyera mofiirira kapena loyera,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:24
5 Mawu Ofanana  

Ndipo padzakhala m'malo mwa zonunkhiritsa mudzakhala zovunda; ndi m'malo mwa lamba chingwe; ndipo m'malo mwa tsitsi labwino dazi; m'malo mwa chovala chapachifuwa mpango wachiguduli; zipsera m'malo mwa ukoma.


ndipo wansembe aone, ndipo taonani, ngati pali chotupa choyera pakhungu, ndipo chasanduliza tsitsi likhale loyera, ndipo pachotupa pali mnofu wofiira,


ndipo padali chilonda pali chotupa choyera, kapena chikanga chotuuluka, pamenepo achionetse kwa wansembe; ndipo wansembe aone,


Koma ngati chikanga chaima pomwepo, chosakula, ndicho chipsera cha chilonda; ndipo wansembe amutche woyera.


pamenepo wansembe achione; ndipo taonani, ngati tsitsi la chikanga lasanduka lotuwa, ndipo chioneka chakumba kubzola khungu; pamenepo ndilo khate lobuka m'kupsamo; ndipo wansembe azimutcha wodetsedwa ndi nthenda yakhate.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa