Levitiko 13:22 - Buku Lopatulika22 ndipo ngati chapitirira khungu, wansembe amutche wodetsedwa; ndilo khate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 ndipo ngati chapitirira khungu, wansembe amutche wodetsedwa; ndilo khate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Nthendayo ikafalikira pa khungu, wansembe amutchule wodwalayo kuti ndi woipitsidwa, limenelo ndi khate. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ngati nthendayo ikufalikira pa khungu, wansembe alengeze kuti munthuyo ndi wodetsedwa. Limeneli ndi khate. Onani mutuwo |