Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:19 - Buku Lopatulika

19 ndipo padali chilonda pali chotupa choyera, kapena chikanga chotuuluka, pamenepo achionetse kwa wansembe; ndipo wansembe aone,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 ndipo padali chilonda pali chotupa choyera, kapena chikanga chotuuluka, pamenepo achionetse kwa wansembe; ndipo wansembe aone,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 ndipo pamene panali chithupsacho pakatuluka zotupatupa zoyera kapena banga loyera mofiirira, aziwonetse kwa wansembe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 ndipo pamalo pamene panali chithupsacho pakatuluka chotupa choyera kapena banga loyera mofiirira, munthuyo ayenera kukadzionetsa kwa wansembe.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:19
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene thupi lili ndi chilonda pakhungu pake, ndipo chapola,


ndipo taonani, ngati chioneka chakumba kubzola khungu, ndipo tsitsi lake lisanduka lotuwa, pamenepo wansembe amutche wodetsedwa; ndiyo nthenda yakhate yabuka m'chilondamo.


Kapena pamene thupi lidapsa ndi moto pakhungu pake, ndipo mnofu wofiira wakupsawo usanduka chikanga chotuuluka, kapena chotuwa;


Koma ngati pali nthenda yotuuluka pakati pa dazi lake la pamutu, kapena la pamphumi, ndipo khate lilikubuka pakati pa dazi lake la pamutu, kapena la pamphumi.


Pamenepo wansembe azimuona, ndipo taonani, ngati chotupa chake cha nthenda chili chotuuluka pa dazi la pamutu wake, kapena la pamphumi pake, monga maonekedwe a khate pa khungu la thupi;


naone nthendayo, ndipo taonani, nthenda ikakhala yosumbudzuka m'makoma a nyumba yobiriwira kapena yofiira, ndipo maonekedwe ake yakumba kubzola khoma;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa