Levitiko 13:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo pamene thupi lili ndi chilonda pakhungu pake, ndipo chapola, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo pamene thupi lili ndi chilonda pakhungu pake, ndipo chapola, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 “Pa khungu la munthu wodwalayo pakakhala chithupsa choti chidapola, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “Ngati pa khungu la munthu wodwalayo pali chithupsa chimene chinapola kale, Onani mutuwo |