Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:17 - Buku Lopatulika

17 ndi wansembe amuone, ndipo taonani, ngati nthenda yasandulika yotuwa, wansembe amutche woyera wanthendayo; ndiye woyera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 ndi wansembe amuone, ndipo taonani, ngati nthenda yasandulika yotuwa, wansembe amutche woyera wanthendayo; ndiye woyera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Tsono wansembeyo amuwonetsetse. Zilondazo zikakhala kuti zasanduka zoyera, wansembeyo amutchule munthu wodwalayo kuti ndi wosaipitsidwa. Ndi woyera ameneyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Wansembe amuonetsetse ndipo ngati zilondazo zasanduka zoyera, wansembe amutchule wodwalayo kuti ndi woyera ndipo adzakhala woyera ndithu.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:17
3 Mawu Ofanana  

Kapena mnofu wofiira ukasandukanso, nusandulika wotuwa, afike kwa wansembe,


Ndipo pamene thupi lili ndi chilonda pakhungu pake, ndipo chapola,


nawaze kasanu ndi kawiri iye amene akuti amyeretse khate lake, namutche woyera, nataye mbalame yamoyo padambo poyera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa