Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:16 - Buku Lopatulika

16 Kapena mnofu wofiira ukasandukanso, nusandulika wotuwa, afike kwa wansembe,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Kapena mnofu wofiira ukasandukanso, nusandulika wotuwa, afike kwa wansembe,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Koma zilondazo zikasinthikanso ndi kusanduka zoyera, pamenepo munthu wodwalayo abwere kwa wansembe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Koma zilondazo zikasinthika ndi kusanduka zoyera, munthuyo ayenera kupita kwa wansembe.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:16
7 Mawu Ofanana  

Ndipo wansembe aone mnofu wofiirawo, namutche wodetsedwa; mnofu wofiira ndiwo wodetsa; ndilo khate.


ndi wansembe amuone, ndipo taonani, ngati nthenda yasandulika yotuwa, wansembe amutche woyera wanthendayo; ndiye woyera.


Ndipo panali, pamene Iye anali mumzinda wina, taona, munthu wodzala ndi khate; ndipo pamene anaona Yesu, anagwa nkhope yake pansi, nampempha Iye, nanena, Ambuye, ngati mufuna mungathe kundikonza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa