Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo wansembe aone mnofu wofiirawo, namutche wodetsedwa; mnofu wofiira ndiwo wodetsa; ndilo khate.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo wansembe aone mnofu wofiirawo, namutche wodetsedwa; mnofu wofiira ndiwo wodetsa; ndilo khate.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Tsono wansembe aonetsetse zilondazo, ndipo munthu wodwalayo amtchule kuti ndi woipitsidwa. Zilondazo nzoipitsa poti limenelo ndi khate.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Wansembe aonetsetse zilondazo ndipo alengeze kuti munthuyo ndi wodetsedwa. Zilondazo ndi zodetsedwa ndipo ili ndi khate.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:15
2 Mawu Ofanana  

Koma tsiku lililonse ukaoneka pa iye mnofu wofiira, adzakhala wodetsedwa.


Kapena mnofu wofiira ukasandukanso, nusandulika wotuwa, afike kwa wansembe,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa