Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 13:14 - Buku Lopatulika

14 Koma tsiku lililonse ukaoneka pa iye mnofu wofiira, adzakhala wodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Koma tsiku lililonse ukaoneka pa iye mnofu wofiira, adzakhala wodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Koma pathupi pake pakaoneka zilonda, ndiye kuti munthuyo ndi woipitsidwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Koma pa tsiku limene zilonda zidzaoneka pa iye, munthuyo adzakhala wodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 13:14
3 Mawu Ofanana  

ndipo wansembe aone, ndipo taonani, ngati pali chotupa choyera pakhungu, ndipo chasanduliza tsitsi likhale loyera, ndipo pachotupa pali mnofu wofiira,


pamenepo wansembe aone, ndipo taonani, ngati khate lakuta thupi lake, amutche woyera wanthendayo; patuwa ponsepo; ndiye woyera.


Ndipo wansembe aone mnofu wofiirawo, namutche wodetsedwa; mnofu wofiira ndiwo wodetsa; ndilo khate.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa