Levitiko 13:13 - Buku Lopatulika13 pamenepo wansembe aone, ndipo taonani, ngati khate lakuta thupi lake, amutche woyera wanthendayo; patuwa ponsepo; ndiye woyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 pamenepo wansembe aone, ndipo taonani, ngati khate lakuta thupi lake, amutche woyera wanthendayo; patuwa ponsepo; ndiye woyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 pamenepo wansembeyo aonetsetse. Khatelo likakhala litagwira thupi lonse, wodwalayo amutchule kuti ndi wosaipitsidwa. Thupi lonse lasanduka loyera ndipo munthuyo ndi wosaipitsidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 wansembe amuonetsetse munthuyo, ndipo ngati khatero lagwira thupi lake lonse, wansembe alengeze kuti munthuyo ndi woyera. Popeza kuti thupi lonse lasanduka loyera, munthuyo ndi woyeretsedwa. Onani mutuwo |