Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 11:5 - Buku Lopatulika

5 Ndi mbira, ingakhale ibzikula koma yosagawanika chiboda, muiyese yodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndi mbira, ingakhale ibzikula koma yosagawanika chiboda, muiyese yodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Mbira: imeneyi njonyansa kwa inu, chifukwa ngakhale imabzikula, ziboda zake nzosagaŵikana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ina ndi mbira, ngakhale imabzikula, zipondero zake nʼzosagawikana. Choncho ndi yodetsedwa, musadye.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 11:5
12 Mawu Ofanana  

Iwowa akufa akali biriwiri, ndi moyo wao utayika ngati odetsedwa.


Mapiri aatali ndiwo ayenera zinkhoma; pamatanthwe mpothawirapo mbira.


Mbira ndi mtundu wopanda mphamvu, koma ziika nyumba zao m'matanthwe.


Nyama iliyonse yogawanika chiboda, nikhala yogawanikadi chiboda, ndi yobzikula, imeneyo muyenera kudya.


Koma izi zokha simuyenera kuzidya mwa zobzikulazo, kapena zogawanika chiboda; ngamira, ingakhale ibzikula, koma yosagawanika chiboda, muziiyesa yodetsedwa.


Ndi kalulu, popeza abzikula koma wosagawanika chiboda, mumuyese wodetsedwa.


Ndipo yense akamva mau anga amenewa, ndi kusawachita, adzafanizidwa ndi munthu wopusa, yemwe anamanga nyumba yake pamchenga;


Koma izi zokha simuyenera kuzidya mwa zobzikulazo, kapena zogawanika chiboda: ngamira, ndi kalulu, ndi mbira, popeza zibzikula, koma zosagawanika chiboda, muziyese zodetsa;


akukhala nao maonekedwe a chipembedzo, koma mphamvu yake adaikana; kwa iwonso udzipatule.


Avomereza kuti adziwa Mulungu, koma ndi ntchito zao amkana Iye, popeza ali onyansitsa, ndi osamvera, ndi pa ntchito zonse zabwino osatsimikizidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa