Levitiko 11:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo zokwawa zonse zakukwawa padziko lapansi zikhale zonyansa; musamazidya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo zokwawa zonse zakukwawa pa dziko lapansi zikhale zonyansa; musamazidya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 “Chinthu chilichonse chokwaŵa pansi nchonyansa, ndipo musadye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 “ ‘Chinthu chilichonse chokwawa pansi ndi chonyansa, simuyenera kudya. Onani mutuwo |