Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 11:34 - Buku Lopatulika

34 Chakudya chilichonse chokhala m'mwemo, chokonzeka ndi madzi, chidzakhala chodetsedwa; ndi chakumwa chilichonse m'chotengera chotere chidzakhala chodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Chakudya chilichonse chokhala m'mwemo, chokonzeka ndi madzi, chidzakhala chodetsedwa; ndi chakumwa chilichonse m'chotengera chotere chidzakhala chodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Madzi am'mbiyamo akathira pa chakudya chilichonse, chakudyacho chidzakhala chonyansa. Chakumwa chilichonse cha m'mbiya ya mtundu umenewo chidzakhala chonyansa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Chakudya chilichonse chimene mungadye chikakhala kuti chathiridwa mʼmbiyamo, ndiye kuti chakudyacho chidzakhala chodetsedwa, ndipo madzi akumwa wochokera mʼmbiya zotere ndi wodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 11:34
7 Mawu Ofanana  

Nsembe ya oipa inyansa Yehova; koma pemphero la oongoka mtima limkondweretsa.


Nsembe ya oipa inyansa; makamaka pakudza nayo iwo mwachiwembu.


Maso akunyada, ndi mtima wodzikuza, ndi nyali ya oipa, zili tchimo.


Wochulukitsa chuma chake, pokongoletsa ndi phindu, angokundikira yemwe achitira osauka chisoni.


Ndipo chilichonse cha izi chikagwa m'chotengera chilichonse chadothi, chinthu chokhala m'mwemo chidetsedwa, ndi chotengeracho muchiswe.


Ndipo kanthu ka mtembo wake kakagwa pa zinthu zilizonse zidzakhala zodetsedwa; ngakhale mchembo kapena mphika wovundikika, aziswe; zodetsa izi, muziyese zodetsedwa.


Zonse ziyera kwa iwo amene ayera mtima; koma kwa iwo odetsedwa ndi osakhulupirira kulibe kanthu koyera; komatu zadetsedwa nzeru zao ndi chikumbumtima chao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa