Levitiko 11:25 - Buku Lopatulika25 ndipo aliyense akanyamulako nyama ya mtembo wake azitsuka zovala zake, nadzakhala wodetsedwa kufikira madzulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 ndipo aliyense akanyamulako nyama ya mtembo wake azitsuka zovala zake, nadzakhala wodetsedwa kufikira madzulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Aliyense akanyamula chiwalo chilichonse cha nyama zakufazo, achape zovala zake, komabe akhala woipitsidwa mpaka madzulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Aliyense wonyamula chiwalo chilichonse cha nyama zakufazo ayenera kuchapa zovala zake, ndipo adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Onani mutuwo |