Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 11:22 - Buku Lopatulika

22 dzombe mwa mtundu wake, ndi chirimamine mwa mitundu yake, ndi njenjete mwa mtundu wake ndi tsokonombwe mwa mitundu yake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 dzombe mwa mtundu wake, ndi chirimamine mwa mitundu yake, ndi njenjete mwa mtundu wake ndi tsokonombwe mwa mitundu yake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Pa zimenezo mungathe kudya izi: dzombe la mitundu yonse, atsokonombwe a mitundu yonse, nkhululu za mitundu yonse, ndi ziwala za mitundu yonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Pa zimenezo mungathe kudya izi: dzombe la mitundu yonse, atsokonombwe a mitundu yonse, nkhululu za mitundu yonse, ndi ziwala za mitundu yonse.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 11:22
10 Mawu Ofanana  

Limbitsani manja opanda mphamvu, ndi kulimbitsa maondo a gwedegwede.


Koma muyenera kudya izi mwa zokwawa zonse zakuuluka, zokhala ndi miyendo inai, zokhala ndi miyendo pa mapazi ao, ya kutumpha nayo pansi; mwa zimenezi muyenera kudya izi:


Koma zokwawa zonse zakuuluka, za miyendo inai, muziyese zonyansa.


Ndipo Yohane yekhayo anali nacho chovala chake cha ubweya wangamira, ndi lamba lachikopa m'chuuno mwake; ndi chakudya chake chinali dzombe ndi uchi wakuthengo.


Ndipo Yohane anavala ubweya wa ngamira, ndi lamba lachikopa m'chuuno mwake, nadya dzombe ndi uchi wakuthengo.


Ndipo iye amene ali wofooka m'chikhulupiriro, mumlandire, koma si kuchita naye makani otsutsana ai.


Ndipo ife amene tili olimba tiyenera kunyamula zofooka za opanda mphamvu, ndi kusadzikondweretsa tokha.


Za iye tili nao mau ambiri kuwanena, ndi otivuta powatanthauzira, popeza mwagontha m'makutu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa