Levitiko 11:20 - Buku Lopatulika20 Zokwawa zonse zakuuluka zokhala ndi miyendo inai, muziyesa izi zonyansa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Zokwawa zonse zakuuluka zokhala ndi miyendo inai, muziyesa izi zonyansa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Zonse za miyendo inai, zouluka, nzonyansa kwa inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “ ‘Zowuluka zonse za miyendo inayi ndi zodetsedwa. Onani mutuwo |