Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 11:20 - Buku Lopatulika

20 Zokwawa zonse zakuuluka zokhala ndi miyendo inai, muziyesa izi zonyansa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Zokwawa zonse zakuuluka zokhala ndi miyendo inai, muziyesa izi zonyansa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 “Zonse za miyendo inai, zouluka, nzonyansa kwa inu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 “ ‘Zowuluka zonse za miyendo inayi ndi zodetsedwa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 11:20
14 Mawu Ofanana  

kwa anthu, ndi dzanja lanu, Yehova, kwa anthu a dziko lapansi pano amene cholowa chao chili m'moyo uno, ndipo mimba yao muidzaza ndi chuma chanu chobisika; akhuta mtima ndi ana, nasiyira ana amakanda zochuluka zao.


indwa, ndi chimeza monga mwa mtundu wake, ndi sadzu, ndi mleme.


Koma muyenera kudya izi mwa zokwawa zonse zakuuluka, zokhala ndi miyendo inai, zokhala ndi miyendo pa mapazi ao, ya kutumpha nayo pansi; mwa zimenezi muyenera kudya izi:


Koma zokwawa zonse zakuuluka, za miyendo inai, muziyese zonyansa.


Ndipo iliyonse iyenda yopanda chiboda mwa zamoyo zonse za miyendo inai, muiyese yodetsedwa; aliyense wokhudza mtembo wake adzakhala wodetsedwa kufikira madzulo.


Palibe munthu angathe kukhala kapolo wa ambuye awiri: pakuti pena adzamuda mmodziyo, ndi kukonda winayo; pena adzakangamira kwa mmodzi, nadzanyoza wina. Simungathe kukhala kapolo wa Mulungu ndi wa Chuma.


Koma Petro anati, Iaitu, Mbuye; pakuti sindinadye ine ndi kale lonse kanthu wamba ndi konyansa.


Ndipo zokwawa zonse zakuuluka muziyesa zonyansa; musamazidya.


pakuti Dema wandisiya ine, atakonda dziko lino lapansi, napita ku Tesalonika; Kresike ku Galatiya, Tito ku Dalamatiya.


Koma iwowa zimene sazidziwa azichitira mwano; ndipo zimene azizindikira chibadwire, monga zamoyo zopanda nzeru, mu izi atayika.


Iwo ndiwo opatukitsa, anthu a makhalidwe achibadwidwe, osakhala naye Mzimu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa