Levitiko 11:2 - Buku Lopatulika2 Nenani ndi ana a Israele, ndi kuti, Izi ndi zamoyo zimene muyenera kumadya mwa nyama zonse zili padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nenani ndi ana a Israele, ndi kuti, Izi ndi zamoyo zimene muyenera kumadya mwa nyama zonse zili pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Auzeni Aisraele kuti nyama zimene angathe kudya pakati pa nyama zonse za pa dziko lapansi ndi izi: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Awuze Aisraeli kuti, ‘Nyama zomwe mukhoza kudya mwa nyama zonse za dziko lapansi ndi izi: Onani mutuwo |