Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 11:19 - Buku Lopatulika

19 indwa, ndi chimeza monga mwa mtundu wake, ndi sadzu, ndi mleme.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 indwa, ndi chimeza monga mwa mtundu wake, ndi sadzu, ndi mleme.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 indwa, zimeza za mitundu yonse, nsadzu ndi mleme.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 indwa, zimeza za mitundu yonse, nsadzu ndi mleme.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 11:19
7 Mawu Ofanana  

Phiko la nthiwatiwa likondwera, koma mapiko ndi nthenga zake nzofatsa kodi?


m'mwemo mbalame zimanga zisa zao; pokhala chumba mpa mitengo ya mikungudza.


Tsiku limenelo munthu adzataya kumfuko ndi kumileme mafano ake asiliva ndi agolide amene anthu anampangira iye awapembedze;


tsekwe, vuwo, ndi dembo;


Zokwawa zonse zakuuluka zokhala ndi miyendo inai, muziyesa izi zonyansa.


Pamenepo ndinakweza maso anga, ndinapenya, ndipo taonani, anatuluka akazi awiri, ndi m'mapiko mwao munali mphepo; ndipo anali nao mapiko ngati mapiko a chumba, nanyamula efayo pakati padziko ndi thambo.


ndi indwa, ndi chimeza, monga mwa mtundu wake, ndi sadzu, ndi mleme.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa