Levitiko 11:11 - Buku Lopatulika11 inde muziyese zonyansa; musamadya nyama zao; mitembo yao zikunyansireni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 inde muziyese zonyansa; musamadya nyama zao; mitembo yao zikunyansireni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Zimenezo zikhale zonyansa kwa inu, ndipo musadye. Zikafa zikhalebe zonyansa kwa inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pakuti zimenezi ndi zodetsedwa kwa inu, nyama yake musadye, ndipo zikafa zikhalebe zodetsedwa kwa inu. Onani mutuwo |