Levitiko 10:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo Aroni analankhula ndi Mose, nati, Taonani, lero abwera nayo nsembe yao yauchimo ndi nsembe yao yopsereza pamaso pa Yehova; ndipo zandigwera zotere; ndikadadya nsembe yauchimo lero, kukadakomera kodi pamaso pa Yehova? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo Aroni analankhula ndi Mose, nati, Taonani, lero abwera nayo nsembe yao yauchimo ndi nsembe yao yopsereza pamaso pa Yehova; ndipo zandigwera zotere; ndikadadya nsembe yauchimo lero, kukadakomera kodi pamaso pa Yehova? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ndipo Aroni adauza Mose kuti, “Taonani, lero anthu apereka nsembe yao yopepesera machimo ndi nsembe yao yopsereza pamaso pa Chauta. Komabe zinthu zoopsa zoterezi zandigwera ine. Nanga ndikadadya zopereka za nsembe yopepesera machimo lero, kodi Chauta akadakondwa?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Aaroni anamuyankha Mose kuti, “Lero anthu apereka nsembe yawo yopepesera machimo ndiponso nsembe yawo yopsereza pamaso pa Yehova komabe zinthu zoterezi zandichitikira. Kodi Yehova akanakondwa ndikanadya nsembe yopepesera machimo lero?” Onani mutuwo |