Levitiko 10:18 - Buku Lopatulika18 Taonani, sanalowe nao mwazi wake m'malo opatulika m'katimo; mukadaidyera ndithu m'malo opatulika, monga ndinakuuzani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Taonani, sanalowe nao mwazi wake m'malo opatulika m'katimo; mukadaidyera ndithu m'malo opatulika, monga ndinakuuzani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Chifukwa magazi ake sadaloŵe nawo m'katikati mwa malo oyera kwambiri, mukadayenera kudyera zimenezi pa malo oyera, monga momwe ndidalamulira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pakuti magazi ake sanalowe nawo ku Malo Wopatulika, mukanadya nyama ya mbuziyo pa malo wopatulikawo monga Yehova analamulira.” Onani mutuwo |