Levitiko 10:10 - Buku Lopatulika10 ndi kuti musiyanitse pakati pa zopatulika ndi zinthu wamba, ndi pakati pa zodetsedwa ndi zoyera; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndi kuti musiyanitse pakati pa zopatulika ndi zinthu wamba, ndi pakati pa zodetsedwa ndi zoyera; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Muzisiyanitsa pakati pa zinthu zoyera ndi zinthu wamba, ndiponso pakati pa zinthu zonyansa ndi zinthu zoyenera pa zachipembedzo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Muzisiyanitsa pakati pa zinthu zopatulika ndi zinthu wamba, pakati pa zinthu zodetsedwa ndi zinthu zoyeretsedwa, Onani mutuwo |