Levitiko 1:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo chopereka chake cha kwa Yehova chikakhala nsembe yopsereza ya mbalame, azibwera nacho chopereka chake chikhale cha njiwa, kapena cha maunda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo chopereka chake cha kwa Yehova chikakhala nsembe yopsereza ya mbalame, azibwera nacho chopereka chake chikhale cha njiwa, kapena cha maunda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ngati munthu apereka kwa Chauta nsembe yopsereza ya mbalame, ikhale njiŵa kapena nkhunda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “ ‘Koma ngati chopereka kwa Yehova ndi nsembe yopsereza ya mbalame, ndiye ikhale njiwa kapena mawunda. Onani mutuwo |